У нас вы можете посмотреть бесплатно SAMEER SULEMAN WAYAMBITSA MAPOKOSO KU PARLIAMENT POMWE WANENA KUTI SONA YA A CHAKWERA NDIYA BODZA или скачать в максимальном доступном качестве, видео которое было загружено на ютуб. Для загрузки выберите вариант из формы ниже:
Если кнопки скачивания не
загрузились
НАЖМИТЕ ЗДЕСЬ или обновите страницу
Если возникают проблемы со скачиванием видео, пожалуйста напишите в поддержку по адресу внизу
страницы.
Спасибо за использование сервиса ClipSaver.ru
Zokambirana za aphungu m'nyumba yamalamulo aziimitsa kaye kwa mphindi makumi atatu. Izi zikutsatira kusamvana mnyumbayi pakati pa aphungu ambali ya boma ndi yotsutsa. Poyamba wachiwiri wa wachiwiri kwa sipikala wa nyumbayi, Aisha Adams anauza phungu wa dera la kum'mwera m'boma la Salima a Christopher Manja kuti atuluke ndikubwera mnyumbayi akatha masiku atatu ati povula jekete lake pomwe amaopsyeza aphungu ena, zinthu zomwe sizidasangalatse ambali ya boma. Kusamvanaku kunabuka phungu wadera lapakati, kummwera chakuvuma munzinda wa Blantyre a Sameer Suleman atatsutsa zomwe mtsogoleri wa dziko lino adayankhula lachisanu lapitali kuti ndizabodza.