У нас вы можете посмотреть бесплатно "Ras Chikomeni:Kukonzekela kuima nawo pa mpando wa u President wa Malawi 🇲🇼 2025 " или скачать в максимальном доступном качестве, видео которое было загружено на ютуб. Для загрузки выберите вариант из формы ниже:
Если кнопки скачивания не
загрузились
НАЖМИТЕ ЗДЕСЬ или обновите страницу
Если возникают проблемы со скачиванием видео, пожалуйста напишите в поддержку по адресу внизу
страницы.
Спасибо за использование сервиса ClipSaver.ru
Lelo pa 11 March 2025, a Ras David Chikomeni Chiwra , akuyenda ulendo wa ndawala mu mzinda wa Lilongwe.Ndicholinga chofuna kupeza ndalama zokwana 10 Miliyoni Malawi Kwacha , yomwe opikisana nawo pa mpando wa president amapeleka ku bungwe loyendesa zisankho. Mchaka cha 2019 a Ras Chikomeni anabwezedwa kokapeleka chikalata chawo ku bungwe loyendesa chisankho chifukwa sanakwanise zina mwa ndondomeko zowayeneleza kuima nawo pa chisankho. Onelani kanema otsatilayi kuti mumve mfundo za a Chikomeni komanso mene akonzekela zisankho zikubwezi ndi zina zomwe asintha kuti asakabwezedwenso ndi bungwe loyendesa zisankho mu dziko lino la Malawi 🇲🇼